Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 13:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mmodzi wa ophunzirawo, amene Yesu ankamukonda,+ anakhala pafupi ndi Yesu.*

  • Yohane 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zitatero, wophunzira amene Yesu ankamukonda kwambiri uja+ anauza Petulo kuti: “Ndi Ambuye!” Simoni Petulo atamva kuti ndi Ambuye, anavala malaya ake akunja, chifukwa anali maliseche,* ndipo analumphira mʼnyanja.

  • Yohane 21:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Petulo anatembenuka nʼkuona wophunzira amene Yesu ankamukonda uja+ akuwatsatira. Wophunzira ameneyu ndi amene pa chakudya chamadzulo chija anatsamira pachifuwa cha Yesu nʼkumufunsa kuti: “Ambuye, ndi ndani amene akufuna kukuperekani?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena