Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:5-8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho iye anaponya ndalama zasiliva zija mʼkachisi nʼkuchoka. Kenako anapita kukadzimangirira.+ 6 Koma ansembe aakulu anatenga ndalama zasilivazo nʼkunena kuti: “Nʼzosaloleka kuti ndalamazi ziikidwe mʼmalo opatulika osungiramo chuma, chifukwa ndi malipiro a magazi.” 7 Atakambirana, anagwiritsa ntchito ndalamazo pogulira munda wa woumba mbiya kuti ukhale manda a alendo. 8 Choncho munda umenewu umatchedwa Munda wa Magazi+ mpaka lero.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena