Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 10:47, 48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 “Anthu awa alandira mzimu woyera ngati mmenenso ife tinalandirira. Ndani amene angaletse kuti asabatizidwe mʼmadzi?”+ 48 Atatero anawalamula kuti abatizidwe mʼdzina la Yesu Khristu.+ Ndiyeno iwo anamupempha kuti akhalebe nawo kwa masiku angapo.

  • Machitidwe 19:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 ndipo anawafunsa kuti: “Kodi munalandira mzimu woyera mutakhala okhulupirira?”+ Iwo anamuyankha kuti: “Ifetu sitinamvepo kuti kuli mzimu woyera.” 3 Iye anawafunsanso kuti: “Nanga munabatizidwa ubatizo wamtundu wanji?” Iwo anayankha kuti: “Tinabatizidwa ubatizo wa Yohane.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena