Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 52:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mapazi a munthu amene akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino ndi okongola kwambiri!+

      Munthu amene akulengeza za mtendere,+

      Amene akubweretsa uthenga wabwino wa zinthu zabwino,

      Amene akulengeza za chipulumutso,

      Amene akuuza Ziyoni kuti: “Mulungu wako wakhala Mfumu.”+

  • Nahumu 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Taonani mapazi a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino.

      Iye akulengeza za mtendere.+

      Iwe Yuda, chita zikondwerero zako.+ Kwaniritsa zimene walonjeza,

      Chifukwa munthu aliyense wopanda pake sadzadutsa pakati pako.

      Munthu wopanda pakeyo adzaphedwa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena