Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 24:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pamene ankadya nawo chakudya,* anatenga mkate nʼkuudalitsa, kenako anaunyemanyema nʼkuyamba kuwagawira.+ 31 Ataona zimenezi, maso awo anatsegukiratu ndipo anamuzindikira, koma iye anazimiririka.+

  • Yohane 21:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yesu anapita kukatenga mkate nʼkuwagawira, ndipo anachitanso chimodzimodzi ndi nsomba. 14 Kameneka kanali kachitatu+ kuti Yesu aonekere kwa ophunzira akewo pambuyo poti waukitsidwa kwa akufa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena