Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 10:44, 45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Pamene Petulo ankalankhula zimenezi, anthu onse amene ankamvetsera mawuwo analandira mzimu woyera.+ 45 Ndipo okhulupirira amene anabwera ndi Petulo aja, amenenso anali odulidwa, anadabwa kwambiri. Iwo anadabwa chifukwa mphatso yaulere ya mzimu woyera inaperekedwanso kwa anthu a mitundu ina.

  • Machitidwe 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma nditangoyamba kulankhula, iwo analandira mzimu woyera ngati mmene zinalilinso ndi ifeyo poyamba paja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena