Yohane 5:28, 29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Musadabwe nazo zimenezi, chifukwa nthawi ikubwera imene onse amene ali mʼmanda achikumbutso adzamva mawu ake+ 29 ndipo adzatuluka. Amene ankachita zabwino adzauka kuti alandire moyo ndipo amene ankachita zoipa adzauka kuti aweruzidwe.+ Yohane 11:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Yesu anamuuza kuti: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira ine, ngakhale atamwalira, adzakhalanso ndi moyo. 1 Akorinto 15:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Tsopano ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa,+ nʼchifukwa chiyani ena a inu akunena kuti akufa sadzaukitsidwa?
28 Musadabwe nazo zimenezi, chifukwa nthawi ikubwera imene onse amene ali mʼmanda achikumbutso adzamva mawu ake+ 29 ndipo adzatuluka. Amene ankachita zabwino adzauka kuti alandire moyo ndipo amene ankachita zoipa adzauka kuti aweruzidwe.+
25 Yesu anamuuza kuti: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira ine, ngakhale atamwalira, adzakhalanso ndi moyo.
12 Tsopano ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa,+ nʼchifukwa chiyani ena a inu akunena kuti akufa sadzaukitsidwa?