Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 17:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno anakumbatira mwanayo katatu ali pabedipo nʼkufuulira Yehova kuti: “Inu Yehova Mulungu wanga, chonde chititsani kuti moyo wa mwanayu ubwerere.” 22 Yehova anamva pemphero la Eliya+ ndipo moyo wa mwanayo unabwerera moti anakhalanso wamoyo.+

  • 2 Mafumu 4:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Elisa atalowa mʼnyumbamo, anapeza mwana wakufayo atamʼgoneka pabedi lake lija.+

  • 2 Mafumu 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kenako anapita pabedipo ndipo anagwada nʼkuweramira mwanayo. Anagunditsa pakamwa pake ndi pakamwa pa mwanayo, maso ake ndi maso a mwanayo komanso manja ake ndi manja a mwanayo. Anakhalabe choncho mpaka thupi la mwanayo linayamba kutentha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena