Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 2:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iye anati:

      “Dzina la Mulungu litamandike mpaka kalekale,*

      Chifukwa nzeru ndi mphamvu ndi zake.+

      21 Iye amasintha nthawi ndi nyengo,+

      Amachotsa mafumu komanso kuika mafumu,+

      Amapereka nzeru kwa anthu anzeru ndiponso amachititsa kuti anthu ozindikira adziwe zinthu.+

  • Mateyu 24:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kunena za tsiku limenelo ndi ola lake, palibe amene akudziwa,+ ngakhale angelo akumwamba kapenanso Mwana, kupatulapo Atate wokha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena