Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma ukaitanidwa, pita ndipo ukakhale kumapeto kwenikweni, kuti munthu amene anakuitana uja akafika adzakuuze kuti, ‘Bwanawe, khala pamalo aulemuwa.’ Zikadzatero udzalemekezeka pamaso pa alendo anzako onse.+

  • Luka 22:24-26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako anayamba kukangana kwambiri za amene anali wamkulu kwambiri.+ 25 Koma Yesu anawauza kuti: “Mafumu a anthu a mitundu ina amachita ulamuliro pa anthu awo, ndipo amene ali ndi mphamvu pa anthuwo amadziwika kuti ndi anthu amene amachitira ena zabwino.+ 26 Inu musakhale otero.+ Koma amene ali wamkulu kwambiri pa nonsenu akhale ngati wamngʼono+ kwambiri pa nonsenu, ndipo amene ali mtsogoleri akhale ngati wotumikira.

  • Yohane 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho ngati ine amene ndi Ambuye komanso Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu,+ inunso mukuyenera kusambitsana mapazi.+

  • Afilipi 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Musamachite chilichonse ndi mtima wokonda mikangano+ kapena chifukwa chodzikuza,+ koma modzichepetsa, muziona kuti ena amakuposani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena