Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kumeneko anapeza Myuda wina dzina lake Akula,+ wa ku Ponto. Iyeyu pamodzi ndi mkazi wake Purisila, anali atangofika kumene kuchokera ku Italy, chifukwa Kalaudiyo anali atalamula Ayuda onse kuti achoke ku Roma. Choncho Paulo anapita kunyumba kwawo.

  • Machitidwe 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano Myuda wina dzina lake Apolo,+ wa ku Alekizandiriya, amene ankalankhula mwaluso, anafika ku Efeso. Iyeyu ankadziwanso bwino Malemba.

  • Machitidwe 18:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Munthu ameneyu anayamba kulankhula molimba mtima musunagoge. Ndiyeno Purisila ndi Akula+ atamumvetsera, anamutenga nʼkumufotokozera njira ya Mulungu molondola.

  • 2 Timoteyo 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Undiperekere moni kwa Purisika ndi Akula+ komanso banja la Onesiforo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena