Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngati mzimu wa amene anaukitsa Yesu uli ndi inu, iye amene anaukitsa Khristu Yesu adzachititsanso matupi anu omwe angathe kufawo+ kukhala ndi moyo,+ pogwiritsa ntchito mzimu wake umene uli ndi inu.

  • Aefeso 1:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 ndi kutinso mudziwe kukula kwa mphamvu zake zopambana zimene wazisonyeza kwa okhulupirirafe.+ Mphamvu zake zazikuluzo zikuonekera muntchito zake, 20 pamene anazigwiritsa ntchito poukitsa Khristu kwa akufa nʼkumukhazika kudzanja lake lamanja+ mʼmalo akumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena