Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 12:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chifukwa cha kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu anandisonyeza, ndikuuza aliyense wa inu kumeneko kuti musamadziganizire kuposa mmene muyenera kudziganizira.+ Koma aliyense aziganiza mwanzeru nʼkumadziweruza mogwirizana ndi chikhulupiriro chimene Mulungu wamupatsa.+

  • 2 Akorinto 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndikuopa kuti ndikadzafika, mwina sindidzakupezani mmene ndikufunira ndipo mwina inenso sindidzakhala mmene mukufunira. Mʼmalomwake, nʼkutheka kuti padzakhala ndewu, nsanje, kukwiyitsana, mikangano, miseche, manongʼonongʼo, kudzitukumula ndiponso chipwirikiti.

  • 3 Yohane 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mpingo wanu ndinaulembera kalata, koma Diotirefe amene amakonda kukhala woyamba pakati panu,+ salemekeza chilichonse chimene tanena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena