Deuteronomo 6:6, 7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Mawu awa amene ndikukulamulani lerowa azikhala pamtima panu, 7 ndipo muziwakhomereza* mumtima mwa ana anu.+ Muzilankhula nawo mawuwo mukakhala pansi mʼnyumba mwanu, mukamayenda pamsewu, mukamagona komanso mukadzuka.+ Miyambo 3:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Mwana wanga, usakane malangizo* a Yehova+Ndipo usanyansidwe ndi kudzudzula kwake,+ Miyambo 19:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Langa mwana wako padakali chiyembekezo,+Ndipo usakhale ndi mlandu wochititsa* kuti afe.+ Miyambo 22:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Phunzitsa mwana kuti aziyenda mʼnjira imene akuyenera kuyendamo.+Ngakhale akadzakalamba sadzachoka mʼnjira imeneyo.+
6 Mawu awa amene ndikukulamulani lerowa azikhala pamtima panu, 7 ndipo muziwakhomereza* mumtima mwa ana anu.+ Muzilankhula nawo mawuwo mukakhala pansi mʼnyumba mwanu, mukamayenda pamsewu, mukamagona komanso mukadzuka.+
11 Mwana wanga, usakane malangizo* a Yehova+Ndipo usanyansidwe ndi kudzudzula kwake,+ Miyambo 19:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Langa mwana wako padakali chiyembekezo,+Ndipo usakhale ndi mlandu wochititsa* kuti afe.+ Miyambo 22:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Phunzitsa mwana kuti aziyenda mʼnjira imene akuyenera kuyendamo.+Ngakhale akadzakalamba sadzachoka mʼnjira imeneyo.+
6 Phunzitsa mwana kuti aziyenda mʼnjira imene akuyenera kuyendamo.+Ngakhale akadzakalamba sadzachoka mʼnjira imeneyo.+