Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Atesalonika 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kodi chiyembekezo chathu kapena chimwemwe chathu nʼchiyani? Kodi mphoto* imene tidzainyadire pamaso pa Ambuye wathu Yesu, pa nthawi ya kukhalapo kwake nʼchiyani? Kodi si inuyo?+

  • 1 Atesalonika 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mulungu wamtendereyo akupatuleni kuti muchite utumiki wake. Ndipo pa mbali zonse abale, mzimu wanu, moyo wanu komanso thupi lanu, zikhale zopanda chilema kapena cholakwa chilichonse, pa nthawi ya kukhalapo kwa Ambuye wathu Yesu Khristu.+

  • 2 Atesalonika 2:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Komabe abale, pa nkhani yokhudza kukhalapo kwa Ambuye wathu Yesu Khristu+ komanso kusonkhanitsidwa kwathu kwa iye,+ tikukupemphani kuti 2 musalole kuti wina aliyense asinthe maganizo anu omwe ndi olondola. Musasokonezeke ngati wina atanena kuti tsiku la Yehova*+ lafika, ngakhale atanena kuti uthengawo ndi wochokera kwa Mulungu,+ kapena atanena kuti anawerenga mʼkalata imene anthu ena akunena kuti ife ndi amene tinalemba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena