Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Akolose 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tachita zimenezi nʼcholinga choti mukhale ndi khalidwe logwirizana* ndi zimene Yehova* amafuna, kuti muzimusangalatsa pa chilichonse, pamene mukupitiriza kubala zipatso pantchito iliyonse yabwino ndi kuwonjezera kumudziwa Mulungu molondola.+

  • 1 Petulo 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mukhale ndi khalidwe labwino pakati pa anthu amʼdzikoli,+ kuti akamakunenani kuti mumachita zoipa, aziona okha zochita zanu zabwino+ kuti kenako adzatamande Mulungu patsiku lake loyendera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena