Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda,+ ndiponso chibonga cha wolamulira sichidzachoka pakati pa mapazi ake, mpaka Silo* atabwera.+ Ndipo mitundu ya anthu idzamumvera.+

  • Mateyu 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Buku la mzere wa makolo a Yesu Khristu,* mwana wa Davide,+ mwana wa Abulahamu:+

  • Mateyu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yuda anabereka Perezi ndi Zera,+ ndipo mayi awo anali Tamara.

      Perezi anabereka Hezironi.+

      Hezironi anabereka Ramu.+

  • Luka 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamene Yesu+ anayamba ntchito yake anali ndi zaka pafupifupi 30.+ Anthu ankadziwa kuti Yesu anali mwana

      wa Yosefe,+

      mwana wa Heli,

  • Luka 3:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 mwana wa Aminadabu,

      mwana wa Arini,

      mwana wa Hezironi,

      mwana wa Perezi,+

      mwana wa Yuda,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena