Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 48:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako anadalitsa Yosefe kuti:+

      “Mulungu woona amene makolo anga Abulahamu ndi Isaki anayenda pamaso pake,+

      Mulungu woona amene wakhala mʼbusa wanga moyo wanga wonse mpaka lero,+

      16 Mngelo amene wakhala akundiwombola ku masoka anga onse,+ adalitse anyamatawa.+

      Anawa azidziwika ndi dzina langa komanso mayina a makolo anga, Abulahamu ndi Isaki,

      Anawa adzachulukane nʼkukhala gulu la anthu ambiri padziko lapansi.”+

  • Genesis 48:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iye anapitiriza kuwadalitsa pa tsikulo+ kuti:

      “Aisiraeli akamadalitsana azidzatchula dzina lako kuti,

      ‘Mulungu akudalitse ngati mmene anadalitsira Efuraimu ndi Manase.’”

      Choncho Isiraeli anapitiriza kuika Efuraimu patsogolo pa Manase.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena