Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Poyankha Yesu anamuuza kuti: “Ndithudi ndikukuuza, munthu sangathe kuona Ufumu wa Mulungu+ ngati sangabadwenso.”*+

  • 1 Petulo 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Atamandike Mulungu wa Ambuye wathu Yesu Khristu, yemwenso ndi Atate wake. Mulungu anatisonyeza chifundo chachikulu pamene anachititsa kuti tibadwenso mwatsopano+ nʼkukhala ndi chiyembekezo chodalirika.+ Zimenezi zinatheka chifukwa cha kuukitsidwa kwa Yesu Khristu.+

  • 1 Petulo 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Inuyo mwabadwanso mwatsopano+ kudzera mʼmawu a Mulungu+ wamoyo ndi wamuyaya. Simunabadwe kuchokera mumbewu yoti ikhoza kuwonongeka, koma mumbewu yomwe singawonongeke.+

  • 1 Yohane 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aliyense amene ali mwana wa Mulungu sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo,+ chifukwa ali ndi mzimu wa Mulungu.* Ndipo sangakhale ndi chizolowezi chochita tchimo, chifukwa ndi mwana wa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena