Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Yohane 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma mawu alionse ouziridwa amene amatsutsa zoti Yesu anabwera monga munthu, amenewo si ochokera kwa Mulungu.+ Mawu amenewo ndi ouziridwa ndi wokana Khristu. Munamva kuti wokana Khristuyu adzalankhula mawu amenewo+ ndipo panopa akuwalankhuladi mʼdzikoli.+

  • 2 Yohane 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komabe samalani chifukwa anthu ambiri opusitsa anzawo ayamba kupezeka mʼdzikoli.+ Anthu amenewa amatsutsa zoti Yesu Khristu anabwera monga munthu.+ Amene amachita zimenezi ndi wopusitsa ena ndiponso wokana Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena