Deuteronomo 33:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Iye anati: “Yehova anabwera kuchokera ku Sinai,+Anawala pa iwo kuchokera ku Seiri. Anawala mwa ulemerero kuchokera kudera lamapiri la Parana,+Ndipo anali ndi angelo ake ambirimbiri,*+Kudzanja lake lamanja kunali asilikali ake.+ Danieli 7:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mtsinje wa moto unkayenda kuchokera kwa iye.+ Panali atumiki okwana 1 miliyoni* amene ankatumikira nthawi zonse ndi atumiki enanso 100 miliyoni* amene ankatumikira pamaso pake nthawi zonse.+ Bwalo la milandu+ linayamba kuzenga mlandu ndipo mabuku anatsegulidwa. Zekariya 14:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Inu mudzathawira kuchigwa chimene chidzakhale pakati pa mapiri anga, chifukwa chigwacho chidzafika mpaka ku Azeli. Mudzathawa ngati mmene munathawira chivomerezi chimene chinachitika mʼmasiku a Uziya, mfumu ya Yuda.+ Ndipo Yehova Mulungu wanga adzabwera limodzi ndi oyera onse.+
2 Iye anati: “Yehova anabwera kuchokera ku Sinai,+Anawala pa iwo kuchokera ku Seiri. Anawala mwa ulemerero kuchokera kudera lamapiri la Parana,+Ndipo anali ndi angelo ake ambirimbiri,*+Kudzanja lake lamanja kunali asilikali ake.+
10 Mtsinje wa moto unkayenda kuchokera kwa iye.+ Panali atumiki okwana 1 miliyoni* amene ankatumikira nthawi zonse ndi atumiki enanso 100 miliyoni* amene ankatumikira pamaso pake nthawi zonse.+ Bwalo la milandu+ linayamba kuzenga mlandu ndipo mabuku anatsegulidwa.
5 Inu mudzathawira kuchigwa chimene chidzakhale pakati pa mapiri anga, chifukwa chigwacho chidzafika mpaka ku Azeli. Mudzathawa ngati mmene munathawira chivomerezi chimene chinachitika mʼmasiku a Uziya, mfumu ya Yuda.+ Ndipo Yehova Mulungu wanga adzabwera limodzi ndi oyera onse.+