Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 28:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Anthu oipa amathawa popanda wowathamangitsa,

      Koma olungama amakhala olimba mtima ngati mkango.*+

  • Yesaya 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chifukwa izi ndi zimene Yehova wandiuza:

      “Mkango umalira moopseza, mkango wamphamvu umalira poteteza nyama imene wagwira.

      Abusa ambirimbiri akaitanidwa kuti adzauthamangitse,

      Suchita mantha ukamva mawu awo

      Kapena kutekeseka chifukwa cha phokoso lawo.

      Mofanana ndi zimenezi, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzatsika kuti achite nkhondo

      Poteteza phiri la Ziyoni ndiponso poteteza phiri lake lalingʼono.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena