Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho inenso ndikukuuza kuti: Iwe ndiwe Petulo+ ndipo pathanthwe+ ili ndidzamangapo mpingo wanga. Mageti a Manda* sadzaugonjetsa.

  • Yohane 6:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Aliyense amene amadya mnofu wanga ndi kumwa magazi anga adzapeza moyo wosatha, ndipo ndidzamuukitsa+ pa tsiku lomaliza.

  • Yohane 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yesu anamuuza kuti: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira ine, ngakhale atamwalira, adzakhalanso ndi moyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena