Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chivumbulutso 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Chilombocho chinakakamiza anthu onse, olemekezeka ndi onyozeka, olemera ndi osauka, mfulu ndi akapolo, kuti aikidwe chizindikiro padzanja lawo lamanja kapena pachipumi pawo.+

  • Chivumbulutso 13:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Apa mʼpamene pakufunika nzeru: Amene ali ndi nzeru awerengere nambala ya chilombocho, chifukwa ndi nambala ya munthu. Nambala yake ndi 666.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena