Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 20:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndikudziwa kuti ine ndikachoka, mimbulu yopondereza idzafika pakati panu+ ndipo sidzasamalira gulu la nkhosa mwachikondi. 30 Ndipo pakati panu anthu ena adzayamba kulankhula zinthu zopotoka kuti apatutse ophunzira aziwatsatira.+

  • 2 Akorinto 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Anthu amenewa ndi atumwi onama, antchito achinyengo ndipo amadzichititsa kuoneka ngati atumwi a Khristu.+

  • 1 Yohane 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Abale okondedwa, musamakhulupirire mawu alionse ouziridwa,*+ koma muzifufuza mawu ouziridwawo* kuti muone ngati alidi ochokera kwa Mulungu,+ chifukwa aneneri abodza* ambiri ayamba kupezeka mʼdzikoli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena