Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 39:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwe udzafera mʼmapiri a ku Isiraeli+ limodzi ndi magulu ako onse a asilikali ndi anthu a mitundu ina amene adzakhale nawe. Ndidzakuperekani kwa mbalame zamitundumitundu zodya nyama ndi zilombo zakutchire kuti mukhale chakudya chawo.”’+

  • Ezekieli 39:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma iwe mwana wa munthu, Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Uza mbalame zamtundu uliwonse ndi zilombo zonse zakutchire kuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere kuno. Zungulirani nsembe yanga imene ndikukukonzerani. Imeneyi ndi nsembe yaikulu mʼmapiri a ku Isiraeli.+ Mukabwera mudzadya nyama ndi kumwa magazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena