Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 62:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Komanso chikondi chokhulupirika ndi chanu, inu Yehova,+

      Chifukwa inu mumabwezera aliyense mogwirizana ndi zochita zake.+

  • Yesaya 40:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Taonani! Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzabwera nʼkuonetsa mphamvu zake,

      Ndipo dzanja* lake lizidzalamulira mʼmalo mwa iyeyo.+

      Mphoto yake ili ndi iyeyo,

      Ndipo malipiro amene amapereka ali pamaso pake.+

  • Aroma 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye adzaweruza aliyense mogwirizana ndi zochita zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena