Saulo ali pa ulendo wa ku Damasiko (1-9)
Hananiya anatumizidwa kuti akathandize Saulo (10-19a)
Saulo analalikira za Yesu ku Damasiko (19b-25)
Saulo anapita ku Yerusalemu (26-31)
Petulo anachiritsa Eneya (32-35)
Dolika, yemwe anali wopatsa, anaukitsidwa (36-43)