Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 1622
  • Zimene Zili M‘buku la Hagai

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili M‘buku la Hagai
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Mfundo Zazikulu za M’mabuku a Hagai ndi Zekariya
    Nsanja ya Olonda—2007
  • “Ine Ndili Nanu”
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Onse Alemekeze Yehova!
    Nsanja ya Olonda—1997
  • “Ndidzagwedeza Mitundu Yonse ya Anthu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili M‘buku la Hagai

HAGAI

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Anadzudzula anthu chifukwa chosamanganso kachisi (1-11)

      • ‘Kodi ino ndi nthawi yoti inu muzikhala mʼnyumba zokongoletsedwa ndi matabwa?’ (4)

      • “Ganizirani mofatsa zimene mukuchita” (5)

      • Kudzala zambiri nʼkukolola zochepa (6)

    • Anthu anamvera mawu a Yehova (12-15)

  • 2

    • Kachisi wachiwiri adzadzaza ndi ulemerero (1-9)

      • Kugwedeza mitundu yonse ya anthu (7)

      • Zinthu zamtengo wapatali zochokera ku mitundu ya anthu zidzabwera (7)

    • Madalitso obwera chifukwa chomanganso kachisi (10-19)

      • Chopatulika sichingachititse kuti chodetsedwa chikhale chopatulika (10-14)

    • Uthenga wopita kwa Zerubabele (20-23)

      • “Ndidzachititsa kuti ukhale ngati mphete yodindira” (23)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena