Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g88 9/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1988
Galamukani!—1988
g88 9/8 tsamba 2

Tsamba 2

Ndi kugwa kwa mabanja ndi mikhalidwe yonyonyotsoka m’masukulu, achichepere avutika. Ngakhale mfuti, mipeni, ndi anamgoneka zakhala zofala m’masukulu a mizinda yaikulu. Kodi nchiyani chimene chiri mathayo ochepera a masukulu ndi makolo m’kuphunzitsa ndi kulera ana? Kodi nchiyani chimene achichepere amafunikira kwenikweni kuchokera kwa makolo awo? Kodi ndi ntchito ya kunyumba yotani imene makolo ayenera kuchita ngati ana awo ati akhale achikulire achipambano?

Chiwopsyezo cha kuwonongedwa kotheratu kwa nyukliya chawopsyeza mtundu wa anthu kwa zaka zoposa makumi anayi. Kuyambitsidwa kwa posachedwapa kwa mtendere, ngakhale kuli tero, kwadzetsa ziyembekezo kaamba ka kuleka kugwiritsiridwa ntchito kotheratu kwa zida. Kodi ziyembekezo zoterozo ziri zenizeni motani? Galamukani! tsopano ikuyang’ana pa nsonga zocholowanacholowana zozungulira nkhani ya kusagwiritsira ntchito zida za nyukliya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena