Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g89 5/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1989
Galamukani!—1989
g89 5/8 tsamba 2

Tsamba 2

“Nduna za ku Latin America tsopano zikuchenjeza kuti m’dziko limodzi pambuyo pa linzake, kugwa kwa miyezo ya kakhalidwe kukuyambitsa kupanda chiyembekezo komwe kukuyamba kusinthira ku kugwa kowopsya kwa ndale zadziko.”—The New York Times, November 29, 1988.

Mkati mwa ma 1980, mamiliyoni a anthu—omwe anali kale osauka mosowa chochita—awona kukwera kwa mtengo wa zinthu kukutsiriza ndalama zawo zochepa zomwe amapezazo ngakhale mopitirira. Kwa iwo, siliri kokha funso la kuchita ndi mtengo wa kakhalidwe koma, m’malomwake, nkhani ya kulimbana kuti afikiritse mtengo wa chipulumuko. Kodi mwawona kukwera mitengo kwa zakudya zofunikira m’dziko lanu? Kodi icho chikuwoneka ngati kuti thumba lanu la zinthu zogula likucheperachepera kaamba ka unyinji wa ndalama zimene mumawononga? Kenaka, mofanana ndi anthu ena ambiri, mukudziŵa kuchokera ku chokumana nacho kuti mtengo wa kakhalidwe ukuwonjezereka.

Kodi pali yankho?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena