Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 5/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 5/8 tsamba 2

Tsamba 2

M’zaka makumi oŵerengeka apita, munthu wasankha njira yamoyo imene yatulukapo m’kuipitsa kwakukulukulu kwa malo okhalamo zamoyo a dziko lapansi—nthaka, mitsinje, nyanja, ndi mlengalenga zaikidwa paizoni. Vutolo liridi la mitundu yonse. Monga mmene papa ananenera muuthenga wake wa Tsiku Ladziko la Mtendere (January 1, 1990) kuti: “M’zochitika zambiri ziyambukiro za malo okhalamo ndi zamoyo zimapitirira malire a Dziko limodzi palokha ; chotero yankho silingapezedwe kotheratu pa mlingo wamtundu.”—L’Osservatore Romano, December 18-26, 1989.

Kusasamala kwa munthu ponena za mtsogolo mwake kumasiyana ndi chisamaliro cha Mulungu kaamba ka dziko lapansi, limene, ndiiko komwe, liri chilengedwe chake. (Yesaya 45:18) Kodi dziko laudongo nlothekera? Ngati nditero, motani ndipo liti? Nkhani zathu zapachikuto zikuyankha mafunso ameneŵa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena