Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g97 3/8 tsamba 32
  • Usiku Woyenera Kuukumbukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Usiku Woyenera Kuukumbukira
  • Galamukani!—1997
Galamukani!—1997
g97 3/8 tsamba 32

Usiku Woyenera Kuukumbukira

SANDE, MARCH 23, 1997

USIKUWO Yesu Kristu asanafe, anayambitsa pamodzi ndi atumwi ake chikumbutso cha imfa yake. Ali pachakudya chopepuka pamene anagwiritsira ntchito vinyo ndi mkate wopanda chotupitsa monga zizindikiro, Yesu analamula kuti: “Chitani ichi chikumbukiro changa.”—Luka 22:19.

Mboni za Yehova zikukupemphani mokoma mtima kuti mudzachite nazo pamodzi Chikumbutso cha chaka ndi chaka chimenechi. Chaka chino chidzachitidwa dzuŵa litaloŵa pa Sande, March 23, deti limene limagwirizana ndi Nisani 14 pa kalenda yamwezi ya Baibulo. Chonde funsani Mboni za Yehova za kwanuko ponena za malo enieni osonkhanira ndi nthaŵi yake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena