Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g02 11/8 tsamba 32
  • Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa!
  • Galamukani!—2002
Galamukani!—2002
g02 11/8 tsamba 32

Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa!

• Kodi N’chifukwa Ninji Makolo Anga Samandimvetsetsa?

• Kodi N’chifukwa Ninji Amayi ndi Atate Analekana?

• Kodi Ndingapange Motani Mabwenzi Enieni?

• Kodi N’chifukwa Chiyani Ndimachita Tondovi Kwambiri?

• Kodi N’chifukwa Chiyani Achichepere Samaleka Kundivutitsa?

• Bwanji Ponena za Kugonana

Buku lakuti Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza n’losiyana ndi mabuku ena a achinyamata. Linalembedwa atakambitsirana ndi achinyamata ambirimbiri padziko lonse. Ndipo mayankho ake, omwe ngochokera m’Baibulo lomwe ndi Mawu a Mulungu, amathandizadi! Mafunso ali pamwambaŵa ndi ena chabe mwa mafunso amene amayankhidwa m’buku la masamba 320 limeneli.

Kuti mulandire buku lanu, mungathe kulemba zofunika m’kabokosi aka n’kukatumiza ku adiresi imene ili pomwepo kapena ku adiresi yoyenera imene ili pa tsamba 5 la magazini ino.

□ Nditumizireni buku la Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza.

□ Chonde nditumizireni munthu kuti ayambe kuchita nane phunziro la Baibulo lapanyumba laulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena