Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g05 2/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2005
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndinu Dr. Livingstone, Eti?”
    Galamukani!—2005
  • Zimene Tingachite Kuti Tisamapanikizike Kwambiri
    Galamukani!—2010
  • Kupanikizika N’koopsa Kwambiri
    Galamukani!—2010
  • Kupanikizika Maganizo Kwabwino ndi Koipa
    Galamukani!—1998
Onani Zambiri
Galamukani!—2005
g05 2/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 8, 2005

Zimene Mungachite Kuti Moyo Wanu Usakhale Wopanikizika

Akatswiri ambiri akukhulupirira kuti kukhala ndi moyo wopanikizika kungawononge kwambiri thanzi la munthu. Kodi zinthu zina zimene zimachititsa moyo kukhala wopanikizika masiku ano n’ziti? Werengani nkhani zofotokoza zinthu zina zomwe mungachite kuti muchepetse kupanikizika pamoyo wanu.

3 Kusowa Mtendere Chifukwa cha Moyo Wopanikizika

4 Zimene Zimachititsa Moyo Kukhala Wopanikizika ndi Zotsatirapo Zake

7 Pali Zimene Mungachite Kuti Moyo Wanu Usakhale Wopanikizika

17 Zimene Zikuchitikira Madokotala M’dziko Limene Likusinthali

19 Madokotala Amakumana N’zambiri

22 Kodi Udokotala uli ndi Tsogolo Lotani?

26 Kodi Mafoni A M’manja ndi Abwino Kapena ndi Oipa?

29 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Ndiyenera Kutani Anthu Ena Akandiuza Mavuto Awo?

32 Buku la Achinyamata Limene Ambiri Amaliyamikira

Kupatsa Ana Chisamaliro Chimene Amafunikira 12

Kodi makolo ayenera kuchita chiyani kuti apatse ana awo chisamaliro chimene amafunikira?

“Ndinu Dr. Livingstone, Eti?” 14

Kukumana kwa Stanley ndi Livingstone kunali kochititsa chidwi kwambiri, komanso kunali kothandiza m’njira zina. Onani zifukwa zomwe ntchito ya amuna awiri amenewa yakhudzira kwambiri miyoyo ya anthu ochuluka.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

From the book Missionary Travels and Researches in South Africa, 1858

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena