Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 3/09 tsamba 32
  • Tsiku Loyenera Kulikumbukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsiku Loyenera Kulikumbukira
  • Galamukani!—2009
Galamukani!—2009
g 3/09 tsamba 32

Tsiku Loyenera Kulikumbukira

Chonde Mudzakhale Nafe—Lachinayi pa April 9, 2009

Usiku woti aphedwa mawa, Yesu Khristu anayambitsa mwambo wokumbukira imfa yake. Pamwambowu, iye anagwiritsa ntchito vinyo ndi mkate wopanda chofufumitsa zomwe zimaimira magazi ndiponso thupi lake lopanda uchimo. Kenako Yesu analamula kuti: “Muzichita zimenezi pondikumbukira ine.”—Luka 22:19.

Ife Mboni za Yehova timamvera lamulo limeneli ndipo tikukupemphani kuti mudzakhale nafe pamwambo umenewu chaka chino. Mungafunse Mboni za Yehova za m’dera lanu kuti mudziwe nthawi yeniyeni ndiponso malo amene kudzachitikire mwambowu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena