Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sg tsamba 3-4
  • Zam’katimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zam’katimu
  • Buku Lolangiza la Sukulu ya Utumiki Wateokalase
Buku Lolangiza la Sukulu ya Utumiki Wateokalase
sg tsamba 3-4

Zam’katimu

TSAMBA PHUNZIRO

5 1 Kulankhula Mawu Okondweretsa a Choonadi

9 2 Sukulu ya Utumiki Wateokalase Imapindulitsa

14 3 Baibulo—Buku Lathu—Lalikulu Lophunzira

19 4 Mmene Tingaŵerengere ndi Kukumbukira

24 5 Khalani Mmvetseri Wabwino

29 6 ‘Chitani Khama Kuŵerenga Poyera’

33 7 Phunziro Limapindulitsa

39 8 Phindu la Kukonzekera

44 9 Kukonza Autilaini

49 10 Kukulitsa Luso Lophunzitsa

54 11 Kukhala ndi Kalankhulidwe Kabwino Tsiku ndi Tsiku

58 12 Kulankhula Kochokera m’Maganizo ndi Kulankhula Mwadzidzidzi

63 13 Kuwongolera Kamvekedwe ka Mawu ndi Kugwiritsa Ntchito Cholankhulira

69 14 Khalani Osamala Komanso Olimba

73 15 Kuwafika Pamtima Omvetsera Anu

78 16 Makambirano Olimbikitsa

84 17 Kalembedwe ka Makalata

90 18 Kuwongolera Mayankho Anu

96 19 Kugwiritsa Ntchito Sukulu Kuwongolera Utumiki Wakumunda

100 20 Uphungu Umalimbikitsa

108 21 Mfundo Zopatsa Chidziŵitso, Zofotokozedwa Momveka Bwino

113 22 Mawu Oyamba Ogwira Mtima

116 23 Mphamvu ya Mawu ndi Kupuma

122 24 Kulozera Maganizo a Omvetsera ku Baibulo

126 25 Kuŵerenga Malemba ndi Kuwatanthauzira

130 26 Ntchito ya Kubwereza ndi Manja

133 27 Kugogomeza Mutu wa Nkhani ndi Mfundo Zazikulu

138 28 Kuyendera Limodzi ndi Omvetsera ndi Ntchito ya Notsi

142 29 Kulankhula Nkhani Mosadodoma, Mokambirana Komanso Motchula Bwino Mawu

149 30 Kulankhula Nkhani Kogwirizanika

153 31 Khutiritsani Omvetsera Anu, Lingalirani Nawo

158 32 Kugogomeza Ganizo ndi Kusinthasintha Mawu

163 33 Kuonetsa Kutengeka Mtima ndi Mzimu Waubwenzi

168 34 Mafanizo Oyenerera

172 35 Kugwirizanitsa Nkhani ndi Utumiki Wakumunda

175 36 Mawu Omalizira Oyenera ndi Kusunga Nthaŵi

181 37 Kukhazikika Maganizo ndi Maonekedwe a Munthu

188 38 Kupita Kwanu Patsogolo Kuonekere

CHIDZIŴITSO: Baibulo limene tagwiritsa ntchito m’buku lino ndi Revised Nyanja (Union) Version, kusiyapo ngati tasonyeza lina. Komabe tatsatira kalembedwe ka orthography yatsopano. Pamene mawu ogwidwa atsatiridwa ndi NW, matembenuzidwewo ali a New World Translation of the Holy Scriptures—With References.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena