Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • re tsamba 320
  • “Pitiriza Kutsatira Zimene Unaphunzira”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Pitiriza Kutsatira Zimene Unaphunzira”
  • Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
re tsamba 320

“Pitiriza Kutsatira Zimene Unaphunzira”

Mtumwi Paulo analemba mawu amenewa kwa Timoteyo, amene anali wachinyamata. (2 Timoteyo 3:14) Pamene mwawerenga buku lino, mwadziwa zinthu zambiri zabwino zimene Mulungu wakonzera anthu amene amamukonda. Koma muyenera kupitiriza kupita patsogolo mwauzimu. Anthu a Mboni za Yehova adzakhala okondwa kukuthandizani kuchita zimenezi, ngati simunayambe kale kuthandizidwa mwanjira imeneyi. Ngati mukufuna kudziwa zambiri, kapena ngati mukufuna kuti munthu wa Mboni za Yehova azibwera kunyumba kwanu kudzaphunzira nanu Baibulo kwaulere, ingolembani kalata kwa Mboni za Yehova pogwiritsa ntchito adiresi yoyenera pa maadiresi amene ali m’munsiwa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena