Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp2 tsamba 11
  • Zigawo Zabukuli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zigawo Zabukuli
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
yp2 tsamba 11

Zigawo Zabukuli

M’bukuli muli . . .

MALEMBA

amene akufotokoza mfundo yaikulu

MFUNDO YOTHANDIZA

izi ndi mfundo zokuthandizani kuti zinthu zizikuyenderani bwino

KODI MUKUDZIWA . . .

zimenezi ndi mfundo zokuthandizani kuganiza

ZOTI NDICHITE

pamenepa muzilembapo zimene mukufuna kuchita pogwiritsa ntchito zimene mwawerenga

MUKUGANIZA BWANJI?

awa ndi mafunso okuthandizani kunena maganizo anu pa zimene mwawerenga

Komanso Muli . . .

MFUNDO ZANGA

tsamba limeneli likupezeka kumapeto kwa chigawo chilichonse ndipo muzilembapo maganizo anu

CHITSANZO CHABWINO

patsambali pakumakhala nkhani ya munthu wa m’Baibulo woti timutsanzire

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena