Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 98
  • Fesani Mbewu za Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fesani Mbewu za Ufumu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kufesa Mbewu za Ufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizifesa Mbewu za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mapindu a Kukonda Mawu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1999
  • ‘Mulungu Ndi Amene Amakulitsa’!
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 98

Nyimbo 98

Fesani Mbewu za Ufumu

Losindikizidwa

(Mateyu 13:4-8)

1. Akapolonu a Yehova

Amene mwadzipereka,

Bwerani kuntchito ya ’Mbuye

Ndipo muzimutsanzira.

Muzifesa mbewu za cho’nadi

M’mitima ya omvetsera.

Mukakhulupirika kwa Mulungu

Inde mudzamulemekeza.

2. Mbewu zina zomwe mufesa

Zidzagweratu pamwala.

Zidzakuladi kwa kanthawi

Pambuyo pake n’kufota.

Minga ikatsamwitsa cho’nadi

Amatengeka ndi dziko.

Zina zidzapeza nthaka yachonde

Ndiponso zidzakula bwino.

3. Kuti ntchito iyende bwino

Khama lanu n’lofunika.

Mukaleza mtima ndi anthu

Angakhozedi kusintha.

Mwa kukhala atcheru mungathe

Kuwathetseradi mantha.

Mungakolole zipatso makumi

Atatu kapena kuposa

(Onaninso Mat. 13:19-23; 22:37.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena