Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 20
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Mudalitse Msonkhano Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 20

Nyimbo 20

Dalitsani Msonkhano Wathu!

Losindikizidwa

(Aheberi 10:24, 25)

1. Pamsonkhanowu Yehova,

Tipempha m’tidalitse.

Ndifetu oyamikira,

Mzimu ukhale nafe.

2. M’tithandize polambira,

M’tipatse Mawu anu.

M’tiphunzitse kulalika,

Tikhale achikondi.

3. Mudalitse misonkhano,

Mutipatse mtendere.

Mawu ndi zochita zathu

Zikulemekezeni.

(Onaninso Sal. 22:22; 34:3; Yes. 50:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena