Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lc tsamba 32
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?
Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?
lc tsamba 32
Kadyamsonga, mpendadzuwa, mbalame, chule

Mawu Oyamba

Kodi zamoyo zinachita kulengedwa kapena zinangokhalapo zokha? Anthu ambiri ali ndi maganizo osiyanasiyana pa nkhaniyi. Koma kudziwa zoona zake n’kofunika kwambiri. Kabukuka kamayankha mafunso ngati awa:

  • Kodi dzikoli linapangidwa kuti muzikhala zamoyo?

  • Kodi tingaphunzire chiyani pa zinthu za m’chilengedwe?

  • Kodi zimene anthu amaphunzitsa zoti zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina zili ndi umboni wake?

  • Kodi sayansi imasonyeza kuti nkhani ya m’Baibulo yokhudza kulenga zinthu si yoona?

  • Kodi zimene mumakhulupirira pa nkhaniyi zimakhudza bwanji moyo wanu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena