Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ll tsamba 2-3
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
ll tsamba 2-3

Mawu Oyamba

Mulungu ali ngati bambo amene amakonda kwambiri ana ake. 1 Petulo 5:6, 7

Banja likulowa m’Paradaiso

Mulungu ndi Mlengi wathu, ndipo amatisamalira mwachikondi. Mofanana ndi bambo wanzeru komanso wachikondi amene amalangiza ana ake, Mulungu amaphunzitsa anthu ake padziko lonse zoyenera kuchita kuti akhale ndi moyo wabwino.

Mulungu amatiphunzitsa choonadi chamtengo wapatali chimene chimatisangalatsa ndiponso kutipatsa chiyembekezo.

Mukamamvera Mulungu, adzakutsogolerani ndi kukutetezani, ndiponso adzakuthandizani kuti muthane ndi mavuto amene mukukumana nawo.

Kuwonjezera pamenepo, mudzakhala ndi moyo wosatha.

Mulungu akutiuza kuti: “Bwerani kwa ine. Mvetserani ndipo mudzakhalabe ndi moyo.” Yesaya 55:3

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena