Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp1 tsamba 3
  • Zomwe Zili M’bukuli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zomwe Zili M’bukuli
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Loyamba
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Loyamba
yp1 tsamba 3

Zomwe Zili M’bukuli

M’bukuli Muli . . .

MALEMBA

amene akufotokoza mfundo zikuluzikulu

MFUNDO YOTHANDIZA

izi ndi mfundo zokuthandizani kuti zinthu zizikuyenderani bwino

KODI MUKUDZIWA . . .?

zimenezi ndi mfundo zokuthandizani kuganiza

ZOTI NDICHITE

pamenepa muzilembapo zimene mukufuna kuchita pogwiritsa ntchito zimene mwawerenga

KODI INUYO MUKUGANIZA BWANJI?

awa ndi mafunso okuthandizani kunena maganizo anu pa zimene mwawerenga

Komanso Muli . . .

MFUNDO ZANGA

tsamba limeneli likupezeka kumapeto kwa chigawo chilichonse ndipo muzilembapo maganizo anu

CHITSANZO CHABWINO

patsambali pakumakhala nkhani ya munthu wa m’Baibulo woti timutsanzire

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena