Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rj tsamba 16
  • Mawu Omaliza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Omaliza
  • Bwererani kwa Yehova
Bwererani kwa Yehova
rj tsamba 16

Mawu Omaliza

Kodi mukukumbukira nthawi yomwe munkasangalala ndi Akhristu anzanu? Mwina mukukumbukira misonkhano ikuluikulu kapena ya mpingo imene inakulimbikitsani kwambiri. Mwinanso munasangalala mutalalikira munthu winawake kapena pamene munacheza ndi m’bale kapena mlongo wina. Ngati zili choncho ndiye kuti simunaiwale Yehova ndipo iyenso sanakuiwaleni. Iye amakumbukira zabwino zimene munkachita pomutumikira ndipo akufunitsitsa kukuthandizani kuti mubwerere.

Paja Yehova anati: ‘Inetu ndidzafunafuna nkhosa zanga ndi kuzisamalira. Ndidzasamalira nkhosa zanga ngati mmene amachitira munthu amene amadyetsa gulu la nkhosa zake pamene ali pakati pa nkhosa zimene zinabalalika. Ndidzapulumutsa nkhosazo kuchokera m’malo onse kumene zinabalalikira.’—Ezekieli 34:11, 12.

Chithunzi cha alongo akusangalala pa msonkhano
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena