Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 72-73
  • Mawu Oyamba Gawo 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 6
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Kulanditsidwa ku Igupto Mpaka pa Mfumu Yoyamba ya Israyeli
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Aisiraeli Analowa M’dziko la Kanani
    Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
  • Yehova Amadalitsa Anthu Okhulupirika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Yefita Anasunga Chowinda Chake kwa Yehova
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 72-73
Samisoni wanyamula geti la mzinda wa Gaza

Mawu Oyamba Gawo 6

Aisiraeli atafika m’Dziko Lolonjezedwa ankalambira Mulungu kuchihema. Ansembe ankaphunzitsa Chilamulo ndipo oweruza ndi amene ankatsogolera anthu. Chigawochi chikufotokoza mmene zosankha komanso zochita za munthu zimakhudzira anthu ena. Mwisiraeli aliyense ankafunikira kukonda Yehova komanso anthu ena. Fotokozani mmene zochita za Debora, Naomi, Yoswa, Hana, mwana wamkazi wa Yefita komanso Samueli zinathandizira anthu ena. Tsindikani mfundo yakuti ngakhale anthu a mitundu ina anasankha kugwirizana ndi Aisiraeli chifukwa ankadziwa kuti Mulungu ankawatsogolera. Chitsanzo pa nkhaniyi ndi Rahabi, Rute, Yaeli ndiponso anthu a ku Gibiyoni.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Yehova anagwiritsa ntchito oweruza populumutsa anthu ake modabwitsa

  • Yehova anadalitsa anthu onse okhulupirika omwe ankamudalira

  • Mulungu alibe tsankho, amalandira anthu ochokera mu mtundu uliwonse omwe amamukonda ndi kuchita zabwino

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena