Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 136-137
  • Mawu Oyamba Gawo 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 10
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Kulambira Nkwa Mulungu
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Chikhulupiriro Chawo Chinapulumuka Chiyeso Choopsa
    Samalani Ulosi wa Danieli!
  • Kodi Mulungu Wako Ndani?
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • Sakanagwada
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 136-137
Mfumu Ahasiwero waloza Mfumukazi Esitere ndi ndodo yake

Mawu Oyamba Gawo 10

Yehova ndi Mfumu ya chilengedwe chonse. Iye wakhala akulamulira kuyambira kalekale ndipo sadzasiya. Mwachitsanzo, iye anapulumutsa Yeremiya ataponyedwa m’chitsime kuti afe. Anapulumutsanso Shadireki, Misheki ndi Abedinego m’ng’anjo ya moto ndiponso anapulumutsa Danieli m’dzenje la mikango. Iye anatetezanso Esitere n’cholinga choti apulumutse anthu a mtundu wake. Yehova sadzalola kuti zoipa zizingopitirizabe. Ulosi wonena za chifaniziro chachikulu komanso mtengo waukulu umasonyeza kuti Ufumu wa Yehova udzathetsa mavuto onse ndipo udzalamulira dziko lonse.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Ufumu wa Yehova ndi wamphamvu kuposa boma lililonse la anthu

  • Tiyenera kukhala olimba mtima ngati Esitere ndi Danieli n’kumachita zoyenera kulikonse komwe tili

  • Tikapanikizika ndi mavuto tizidalira kwambiri Yehova ngati mmene anachitira Yeremiya ndi Nehemiya

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena