Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 4/1 tsamba 32
  • April 12 Chikumbutso“

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 12 Chikumbutso“
  • Nsanja ya Olonda—1987
Nsanja ya Olonda—1987
w87 4/1 tsamba 32

April 12 Chikumbutso“

Ndipo mmene adatenga mkate, nayamika, anaunyema, nawapatsa, nanena, ’Ichi ndi thupi langa lopatsidwa chifukwa cha inu. Chitani ichi chikumbukiro changa.’ Ndipo, choteronso chikho, atatha mgonero, nanena, ’Chikho ichi ndi pangano latsopano la mwazi wanga wothiridwa chifukwa cha inu.”’​—Luka 22:19, 20.

Mboni za Yehova zikukuitanani inu kukapezekapo kaamba ka kukumbukira kusunga Chikumbutso kopambana kwambiri kumeneku. Chaka chino tsiku pa kalenda yathu lomwe likugwirizana ndi tsiku limene Yesu anafa liri Sande, April 12, pambuyo pa kulowa kwa dzuwa. Mungapezekepo pa madzulo amenewo pa Nyumba ya Ufumu imene iri kufupi ndi nyumba yanu. Fufuzani ndi Mboni za Yehova za kumaloko kaamba ka nthawi yeniyeni.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena