Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w91 5/15 tsamba 32
  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Nsanja ya Olonda—1991
Nsanja ya Olonda—1991
w91 5/15 tsamba 32

“Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Lomwe liri pamwambalo ndi lonjezo lochokera kwa Mulungu limene latengedwa kukhala mutu wa brosha yochititsa nthumanzi. Kodi lonjezo limenelo limatanthauzanji kwa ife? Kodi lidzakwaniritsidwa motani, ndipo liti? Mungapeze mayankho mwakuŵerenga chofalitsidwa chokongolachi chamasamba 32. Ngati mungakonde kulandira kope, chonde dzazani ndi kutumiza kapepala kali pansipa.

Ndingakonde kulandira brosha yamasamba 32 ya “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano.” (Kunja kwa Zambia, lemberani nthambi ya Watch Tower yakwanuko kaamba ka chidziŵitso. Onani tsamba 2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena