Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w99 3/15 tsamba 32
  • Tsiku Loyenera Kulikumbukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsiku Loyenera Kulikumbukira
  • Nsanja ya Olonda—1999
Nsanja ya Olonda—1999
w99 3/15 tsamba 32

Tsiku Loyenera Kulikumbukira

Madzulo a tsiku loti maŵa lake akafa, Yesu anapereka mkate wopanda chotupitsa ndi chikho cha vinyo kwa atumwi ake ndipo anawauza kuti adye ndi kumwa. Anawauzanso kuti: “Chitani ichi chikumbukiro changa.”​—Luka 22:19.

Chaka chino tsiku lokumbukira chochitika chimenechi ndi Lachinayi, April 1, dzuŵa litaloŵa. Mboni za Yehova padziko lonse lapansi zidzasonkhana usiku wapadera umenewu ndi kuchita Chikumbutso chimenechi m’njira imene Yesu analamula. Mukuitanidwa ndi mtima wonse kudzakhala nafe. Chonde funsani Mboni za Yehova kwanuko kuti zikuuzeni nthaŵi ndi malo a msonkhano wapadera umenewu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena